Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 13:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ndidzalanga dziko lapansi, cifukwa ca kuipa kwao, ndi oipa cifukwa ca mphulupulu zao; ndipo ndidzaletsa kudzikuza kwa onyada, ndidzagwetsa kudzikweza kwa oopsya.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 13

Onani Yesaya 13:11 nkhani