Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 10:31-34 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

31. Madimena ali wothawathawa; okhala m'Gebimu asonkhanakutiathawe.

32. Lero lomwe adzaima pa Nobu; agwedezera dzanja lace pa phiri la mwana wamkazi wa Ziyoni, phiri la Yerusalemu.

33. Taonani, Ambuye Yehova wa makamu adzasadza nthambi moopsya; ndipo zazitari msinkhu zidzadulidwa, ndipo zazitari zidzagwetsedwa.

34. Ndipo adzadula nkhalango za m'thengo ndi citsulo, ndipo Lebano adzagwa ndi wamphamvu.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 10