Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 1:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Kucokera pansi pa phazi kufikira kumutu m'menemo mulibe cangwiro; koma mabala, ndi mikwingwirima, ndi zironda; sizinapole, ngakhale kumangidwa, ngakhale kupakidwa mafuta.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 1

Onani Yesaya 1:6 nkhani