Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 9:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Wanzeru ndani, kuti adziwe ici? ndani iye amene kamwa la Yehova lanena naye, kuti acilalikire? cifukwa cace dziko litha ndi kupserera monga cipululu, kuti anthu asapitemo?

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 9

Onani Yeremiya 9:12 nkhani