Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 8:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Kumina kwa akavalo ace kunamveka ku Dani; dziko lonse linanthunthumira pa kulira kwa akavalo acewo olimba; cifukwa afika, nadya dziko ndi zonse za momwemo; mudzi ndi amene akhalamo.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 8

Onani Yeremiya 8:16 nkhani