Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 7:31 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Namanga akacisi a ku Tofeti, kuli m'cigwa ca mwana wa Hinomu, kuti atenthe m'moto ana ao amuna ndi akazi; cimene sindinauza iwo, sicinalowa m'mtima mwanga.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 7

Onani Yeremiya 7:31 nkhani