Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 6:23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Agwira uta ndi nthungo; ali ankharwe, alibe cifundo; mau ao aphokosera ngati nyanja, akwera pa akavalo; aguba monga anthu ofuna kumenyana nkhondo ndi iwe, mwana wamkazi wa Ziyoni.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 6

Onani Yeremiya 6:23 nkhani