Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 6:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndidzanena ndi yani, ndidzacita mboni kwa yani, kuti amve? Taona khutu lao liri losadulidwa, ndipo sangathe kumva; taona, mau a Yehova awatonzetsa iwo; sakondwera nao.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 6

Onani Yeremiya 6:10 nkhani