Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 52:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo panaoneka caka cacisanu ndi cinai ca ufumu wace mwezi wakhumi, tsiku lakhumi la mwezi, Nebukadirezara mfumu ya ku Babulo anafika, iye ndi nkhondo yace, kuti amenyane ndi Yerusalemu, ndipo anammangira zitando; ndipo anammangira malinga pozungulira pace.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 52

Onani Yeremiya 52:4 nkhani