Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 52:25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndipo m'mudzi anatenga kazembe amene anali woyang'anira anthu a nkhondo ndi amuna asanu ndi awiri a iwo akuona nkhope ya mfumu, amene anapezedwa m'mudzi; ndi mlembi wa kazembe wa nkhondo, amene akamemeza anthu a m'dziko; ndi amuna makumi asanu ndi limodzi a anthu a m'dziko, amene anapezedwa pakati pa mudzi.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 52

Onani Yeremiya 52:25 nkhani