Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 51:56 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

pakuti wakufunkha wafika kwa iye, kwa Babulo, ndi anthu ace olimba agwidwa, mauta ao atyokatyoka, pakuti Yehova ndiye Mulungu wakubwezera, adzabwezera ndithu.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 51

Onani Yeremiya 51:56 nkhani