Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 51:36 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace Yehova atero: Taona, ndidzanenera iwe mlandu wako, ndidzawabwezera cilango cifukwa ca iwe; ndidzaphwetsa nyanja yace, ndidzaphwetsa citsime cace.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 51

Onani Yeremiya 51:36 nkhani