Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 50:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Muwathe ofesa ku Babulo, ndi iwo amene agwira zenga nyengo ya masika; cifukwa ca lupanga losautsa adzatembenukira yense kwa anthu ace, nadzathawira yense ku dziko lace.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 50

Onani Yeremiya 50:16 nkhani