Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 5:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Adzadya zokolola zako, ndi mkate wako, umene ana ako amuna ndi akazi ayenera kudya; adzadya nkhosa zako ndi zoweta zako; adzadya mphesa zako ndi nkhuyu zako; adzapasula ndi lupanga midzi yamalinga yako, imene ukhulupiriramo.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 5

Onani Yeremiya 5:17 nkhani