Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 46:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nenani m'Aigupto, lalikirani m'Migidoli, lalikirani m'Nofi ndi Tapanesi; nimuti, Udziimike, nudzikonzere wekha; pakuti lupanga ladya pozungulira pako.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 46

Onani Yeremiya 46:14 nkhani