Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 44:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo tsopano atero Yehova, Mulungu wa makamu, Mulungu wa Israyeli: Cifukwa canji mucitira miyoyo yanu coipa ici, kudzisadzira nokha amuna ndi akazi, makanda ndi oyamwa, pakati pa Yuda, osakusiyirani mmodzi yense;

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 44

Onani Yeremiya 44:7 nkhani