Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 44:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

kuti otsala a Yuda, amene ananka ku dziko la Aigupto kukhala m'menemo, asapulumuke asatsale ndi mmodzi yense, kuti abwere ku dziko la Yuda, kumene afuna kubwera kuti akhale m'menemo; pakuti adzabwera koma adzapulumuka ndiwo.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 44

Onani Yeremiya 44:14 nkhani