Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 40:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mau amene anadza kwa Yeremiya kucokera kwa Yehova, Nebuzaradani kapitao wa alonda atammasula pa Rama, pamene anamtenga iye womangidwa m'maunyolo pamodzi ndi am'nsinga onse a Yerusalemu ndi Yuda, amene anatengedwa am'nsinga kunka nao ku Babulo.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 40

Onani Yeremiya 40:1 nkhani