Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 4:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mkango wakwera kuturuka m'nkhalango mwace, ndipo woononga amitundu ali panjira, waturuka m'mbuto mwace kuti acititse dziko lako bwinja, kuti midzi yako ipasuke mulibenso wokhalamo.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 4

Onani Yeremiya 4:7 nkhani