Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 37:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Zedekiya mfumu anatuma Yehukali mwana wa Selemiya, ndi Zefaniya mwana wa Maseya wansembe, kwa Yeremiya mneneri, kukanena, Mutipemphereretu kwa Yehova Mulungu wathu.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 37

Onani Yeremiya 37:3 nkhani