Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 37:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

pamenepo Zedekiya mfumu inatuma, ndi kumtenga iye; ndipo mfumu inamfunsa iye m'tseri m'nyumba mwace, niti, Kodi alipo mau ocokera kwa Yehova? Ndipo Yeremiya, anati, Alipo, Anatinso, Mudzaperekedwa m'dzanja la mfumu ya ku Babulo.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 37

Onani Yeremiya 37:17 nkhani