Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 36:23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo panali, pamene Yehudi anawerenga masamba atatu pena anai, mfumu inawadula ndi kampeni ka mlembi, niwaponya m'moto wa m'nkhumbaliromo, mpaka mpukutu wonse unatha kupsa ndi moto wa m'nkhumbaliromo.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 36

Onani Yeremiya 36:23 nkhani