Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 33:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Adza kumenyana ndi Akasidi, koma adzangozidzaza ndi mitembo ya anthu, amene ndawapha m'mkwiyo wanga ndi mu ukali wanga, amene ndabisira mudzi uno nkhope yanga cifukwa ca zoipa zao zonse.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 33

Onani Yeremiya 33:5 nkhani