Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 31:37 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Atero Yehova, Ngati ukhoza kuyesa thambo la kumwamba, ndi kusanthula pansi maziko a dziko, pamenepo ndidzacotsa mbeu zonse za Israyeli cifukwa ca zonse anazicita, ati Yehova.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 31

Onani Yeremiya 31:37 nkhani