Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 3:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pita; nulalikire mau awa kuyang'ana kumpoto, ndi kuti, Bwera iwe Israyeli wobwerera, ati Yehova; sindidzakuyang'anira iwe ndi kukwiya; pakuti Ine ndiri wacifundo, ati Yehova, sindidzakhala nako kukwiya ku nthawi zonse.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 3

Onani Yeremiya 3:12 nkhani