Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 29:32 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

cifukwa cace atero Yehova, Taonani, ndidzalanga Semaya Mnehelamu, ndi mbeu zace; sadzakhala ndi munthu wakukhala mwa anthu awa, sadzaona za bwino ndidzacitira anthu anga, ati Yehova: cifukwa wanena zopikisana ndi Yehova.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 29

Onani Yeremiya 29:32 nkhani