Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 26:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Bwanji mwanenera m'dzina la Yehova, kuti, Nyumba iyi idzafanana ndi Silo, mudzi uwu udzakhala bwinja lopanda wokhalamo? Ndipo anthu onse anamsonkhanira Yeremiya m'nyumba ya Yehova.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 26

Onani Yeremiya 26:9 nkhani