Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 26:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Yehova atero: Ima m'bwalo la nyumba ya Yehova, ndi kunena kwa midzi yonse ya Yuda, imene imadza kudzagwadira m'nyumba ya Yehova, mau onse amene ndikuuza iwe kuti unene kwa iwo; usasiyepo mau amodzi.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 26

Onani Yeremiya 26:2 nkhani