Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 23:38 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma ngati muti, Katundu wa Yehova, cifukwa cace Yehova atero: Cifukwa muti mau awa, Katundu wa Yehova, ndipo ndatuma kwa inu, kuti, Musati, Katundu wa Yehova;

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 23

Onani Yeremiya 23:38 nkhani