Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 22:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Yehova atero: Citani ciweruzo ndi cilungamo, landitsani ofunkhidwa m'dzanja la wosautsa; musacite coipa, musamcitire mlendo ciwawa, kapena ana amasiye, kapena akazi amasiye, musakhetse mwazi wosacimwa pamalo pano.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 22

Onani Yeremiya 22:3 nkhani