Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 22:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace Yehova atero za Yehoyakimu mwana wace wa Yosiya, mfumu ya Yuda: Sadzamlira iye, kuti, Kalanga ine mbale wanga! kapena, Kalanga ine mlongo wanga! Sadzamlira, kuti, Kalanga ine mbuye! kapena, Kalanga ine ulemerero wace!

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 22

Onani Yeremiya 22:18 nkhani