Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 22:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti Yehova atero za Salumu mwana wace wa Yosiya, mfumu ya Yuda, amene analamulira m'malo mwace mwa Yosiya atate wace, amene anaturuka m'malo muno: Sadzabweranso kuno nthawi iri yonse;

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 22

Onani Yeremiya 22:11 nkhani