Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 21:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mau amene anadza kwa Yeremiya kucokera kwa Yehova, pamene Zedekiya mfumu anatuma kwa iye Pasuri mwana wa Malikiya, ndi Zefaniya mwana wace wa Maseya wansembe, akati,

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 21

Onani Yeremiya 21:1 nkhani