Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 17:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Iwe, iwe wekha, udzaleka pa colowa cako cimene ndinakupatsa iwe; ndipo ndidzakutumikiritsa adani ako m'dziko limene sulidziwa; pakuti wakoleza moto m'mkwiyo wanga umene udzatentha ku nthawi zamuyaya.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 17

Onani Yeremiya 17:4 nkhani