Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 14:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Atero Yehova kwa anthu awa, Comwecoakonda kusocerera; sanakaniza mapazi ao; cifukwa cace. Yehova sawalandira; tsopano adzakumbukira coipa cao, nadzalanga zocimwa zao.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 14

Onani Yeremiya 14:10 nkhani