Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 10:25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Tsanulirani ukali wanu pa amitundu osakudziwani Inu, ndi pa mabanja osaitana dzina lanu; pakuti anadya Yakobo, inde, anamudya namutha, napasula mokhalamo mwace.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 10

Onani Yeremiya 10:25 nkhani