Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 10:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Gawo la Yakobo silifanana ndi iwo; pakuti iye ndiye analenga zonse; Israyeli ndiye mtundu wa colowa cace; dzina lace ndi Yehova wa makamu.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 10

Onani Yeremiya 10:16 nkhani