Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Oweruza 3:29-31 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

29. Ndipo anakantha Amoabu nyengo ija anthu zikwi khumi, onsewa anthu amoyo, ndi ngwazi; ndipo sanapulumuka ndi mmodzi yense.

30. Motero anagonjetsa Moabu tsiku lija pansi pa dzanja la Israyeli. Ndipo dziko linapumulazaka makumi asanu ndi atatu.

31. Atapita iye kunali Samagara, mwana wa Anati amene anakantha Afilisti mazana asanu ndi limodzi ndi mtoso wa ng'ombe; nayenso anapulumutsa Israyeli.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 3