Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Oweruza 18:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

koma amuna asanu omukawo kukazonda dziko anakwera nalowako, natenga fano losema, ndi cobvala ca wansembe ndi timafano, ndi fano loyenga; ndi wansembe anaima polowera pa cipata pamodzi ndi amuna mazana asanu ndi limodzi omangira zida za nkhondo m'cuuno.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 18

Onani Oweruza 18:17 nkhani