Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Oweruza 16:30-31 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

30. Nati Samsoni, Ndife nao Afilisti; nadziweramira mwamphamvu; ndipo nyumba idagwa pa akalonga, ndi pa anthu onse anali m'mwemo. Motero akufa amene anawapha pa kufa kwace anaposa amene anawapha akali moyo.

31. Pamenepo anatsika abale ace ndi banja lonse la atate wace, namnyamula, Dakwera naye, namuika pakati pa Zora ndi Esitaoli, m'manda a Manowa atate wace. Ndipo adaweruza Israyeli zaka makumi awiri.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 16