Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Oweruza 16:20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anati, Afilisti akugwera, Samsoni. Nagalamuka iye m'tulo tace, nati, Ndizituruka ngati nthawi zina, ndi kudzitakasika. Koma sanadziwa kuti Yehova adamcokera.

Werengani mutu wathunthu Oweruza 16

Onani Oweruza 16:20 nkhani