15. Ndiwe kasupe wa m'minda,Citsime ca madzi amoyo,Ndi mitsinje yoyenda yocokera ku Lebano.
16. Galamuka, mphepo ya kumpoto iwe, nudze, mphepo iwe ya kumwela;Nuombe pamunda panga, kuti zonunkhiritsa zace ziturukemo.Bwenzi langa mnyamatayo, alowe m'munda mwace,Nadye zipatso zace zofunika.