Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 7:38-42 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

38. cipande cimodzi cagolidi ca masekeli khumi, codzala ndi cofukiza;

39. ng'ombe yamphongo imodzi, nkhosa yamphongo imodzi, mwana wa nkhosa mmodzi wa caka cimodzi, zikhale nsembe yopsereza;

40. tonde mmodzi akhale nsembe yaucimo;

41. ndi nsembe yoyamika, ng'ombe ziwiri, nkhosa zamphongo zisanu, atonde asanu, ana a nkhosa asanu a caka cimodzi; ndico copereka ca Selumiyeli mwana wa Zurisadai.

42. Tsiku lacisanu ndi cimodzi, kalonga wa ana a Gadi, Eliyasafe mwana wa Deyueli:

Werengani mutu wathunthu Numeri 7