Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 4:37 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Awa ndi owerengedwa a mabanja a Akohati, onse akutumikira m'cihema cokomanako, amene Mose ndi Aroni anawawerenga monga mwa mau a Yehova mwa dzanja la Mose.

Werengani mutu wathunthu Numeri 4

Onani Numeri 4:37 nkhani