Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 36:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pofika caka coliza ca ana a Israyeli adzaphatikiza colowa cao ku colowa ca pfuko limene akhalako; cotero adzacotsa colowa cao ku colowa ca pfuko la makolo athu.

Werengani mutu wathunthu Numeri 36

Onani Numeri 36:4 nkhani