Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 35:21-24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

21. kapena kumpanda ndi dzanja lace momuda, kuti wafa, womkanthayo nayenso amuphe ndithu; ndiye wakupha munthu; wolipsa mwazi aphe wakupha munthuyo pomkumika.

22. Koma akampyoza modzidzimuka, osamuda, kapena kumponyera kanthu osamialira,

23. kapena kumponyera mwala wakufetsa munthu, osamuona, namgwetsera uwu, kuti wafa, koma sindiye mdani wace, kapena womfunira coipa;

24. pamenepo msonkhano uziweruza pakati pa wokantha mnzaceyo ndi wolipsa mwaziyo monga mwa maweruzo awa;

Werengani mutu wathunthu Numeri 35