Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 33:38 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Aroni wansembe anakwera m'phiri la Hori pa mau a Yehova, nafa komweko, ataturuka ana a Israyeli m'dziko la Aigupto zaka makumi anai, mwezi wacisanu, tsiku loyamba la mwezi.

Werengani mutu wathunthu Numeri 33

Onani Numeri 33:38 nkhani