Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 31:15-19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

15. Ndipo Mose ananena nao, Kodi mwasunga ndi moyo akazi onse?

16. Taonani, awa analakwitsa ana a Israyeli pa Yehova nilica Peoricija, monga adawapangira Balamu; kotero kuti kunali mliri m'khamu la Yehova.

17. Ndipo tsono iphani amuna onse mwa anawo, iphaninso akazi onse akudziwa mwamuna mogona naye.

18. Koma ana akazi onse osadziwa mwamuna mogona naye, asungeru ndi moyo akhale anu.

19. Ndipo mukhale m'misasa kunja kwa cigono masiku asanu ndi awiri; ali yense adapha munthu, ndi ali yense wakukhudza wophedwa, mudziyeretse tsiku lacitatu ndi lacisanu ndi ciwiri, inu ndi andende anu.

Werengani mutu wathunthu Numeri 31