Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 3:38 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo amene adamanga mahema ao pa khomo la kacisi, kum'mawa, pa khomo la cihema cokomanako koturukira dzuwa, ndiwo Mose ndi Aroni, ndi ana ace amuna, akusunga udikiro wa malo opatulika, ndiwo udikiro wa ana a Israyeli; koma mlendo wakuyandikizako amuphe,

Werengani mutu wathunthu Numeri 3

Onani Numeri 3:38 nkhani