Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 25:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndipo lidzakhala kwa iye, ndi kwa mbeu zace zakumtsata pangano la unsembe wosatha, popeza anacita nsanje cifukwa ca Mulungu wace, anawacitira ana a Israyeli cowatetezera.

Werengani mutu wathunthu Numeri 25

Onani Numeri 25:13 nkhani